Nnwom 25 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 25:1-22

Dwom 25

Dawid dwom.

1Awurade, me Nyankopɔn, wo mu na mede me werɛ hyɛ.

2Wo so, me Nyankopɔn, na mede me ho to,

mma mʼanim ngu ase,

na mma mʼatamfo nso nni me so nkonim.

3Wɔn a wɔde wɔn ho to wo so no mu biara

anim rengu ase da,

mmom, wɔn a wɔyɛ kɔntɔnkye kwa no

anim begu ase.

4Kyerɛ me wʼakwan, Awurade,

na minhu wʼatempɔn.

5Fa wo nokware no so kyerɛkyerɛ me,

efisɛ woyɛ Onyankopɔn, me Gyefo,

na mʼani da wo so daa nyinaa.

6Kae, Awurade, wo mmɔborɔhunu ne wo dɔ kɛse

a ɛwɔ hɔ fi tete no.

7Nkae me mmabun bere mu bɔne

ne mʼatuatew akwan;

kae me sɛnea wʼadɔe te,

Awurade, efisɛ wuye.

8Awurade ye na ɔteɛ;

enti ɔkyerɛkyerɛ nnebɔneyɛfo nʼakwan.

9Ɔde ahobrɛasefo fa ɔkwan pa so

na ɔkyerɛ wɔn nʼapɛde.

10Awurade akwan nyinaa yɛ ɔdɔ ne nokwaredi

ma wɔn a wodi nʼapam mu ahyɛde so.

11Awurade, me bɔne so de,

nanso wo din nti, fa kyɛ me.

12Enti hena ne onipa a osuro Awurade?

Ɔbɛkyerɛ no ɔkwan a wabɔ ama no.

13Obedi yiye wɔ ne nkwanna mu,

na nʼasefo afa asase no sɛ wɔn agyapade.

14Awurade da nʼatirimsɛm adi kyerɛ wɔn a wosuro no;

na ɔma wohu nʼapam.

15Mʼani da Awurade so daa,

efisɛ ɔno nko ara na obeyi mʼanan afi afiri mu.

16Dan wʼani hwɛ me, na dom me,

efisɛ meyɛ ankonam na meyɛ mmɔbɔ.

17Me koma mu dadwen adɔɔso;

yi me dadwen fi me so.

18Hwɛ me haw ne mʼahohiahia

na yi me bɔne nyinaa fi me so.

19Hwɛ sɛnea mʼatamfo adɔɔso

ne ɔtan kɛse a wɔde tan me!

20Bɔ me nkwa ho ban na gye me;

mma mʼanim ngu ase,

efisɛ me guankɔbea ne wo.

21Ma trenee ne nokware mmɔ me ho ban,

efisɛ mʼani da wo so.

22Gye Israel, Onyankopɔn,

fi wɔn haw nyinaa mu.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 25:1-22

Salimo 25

Salimo la Davide.

1Kwa Inu Yehova, ndipereka moyo wanga.

2Ndimadalira Inu Mulungu wanga.

Musalole kuti ndichite manyazi

kapena kuti adani anga andipambane.

3Aliyense amene amayembekezera kwa Ambuye

sadzachititsidwa manyazi

koma achinyengo ndiwo adzachititsidwe manyazi

ndipo sadzakhala ndi chodzitetezera.

4Ndidziwitseni njira zanu Inu Yehova,

phunzitseni mayendedwe anu;

5tsogolereni mʼchoonadi chanu ndi kundiphunzitsa,

pakuti Inu ndinu Mulungu mpulumutsi wanga,

ndipo chiyembekezo changa chili mwa Inu tsiku lonse.

6Kumbukirani Inu Yehova chifundo ndi chikondi chanu chachikulu,

pakuti ndi zakalekale.

7Musakumbukire machimo a ubwana wanga

ndi makhalidwe anga owukira;

molingana ndi chikondi chanu ndikumbukireni ine,

pakuti Inu Yehova ndinu wabwino.

8Yehova ndi wabwino ndi wolungama;

choncho Iye akulangiza ochimwa mʼnjira yake.

9Amatsogolera odzichepetsa kuti achite zolungama

ndipo amawaphunzitsa njira zake.

10Njira zonse za Yehova ndi zachikondi ndi zokhulupirika

kwa iwo amene amasunga zofuna za pangano lake.

11Chifukwa cha dzina lanu, Inu Yehova,

khululukireni mphulupulu zanga, ngakhale kuti ndi zochuluka.

12Tsono ndani munthu amene amaopa Yehova?

Yehova adzamulangiza njira yoti ayitsate.

13Iye adzakhala pa ulemerero masiku ake onse,

ndipo zidzukulu zake zidzalandira dziko ngati cholowa chawo.

14Yehova amawulula chinsinsi chake kwa iwo amene amamuopa;

amawulula pangano lake kwa iwowo.

15Maso anga ali pa Yehova nthawi zonse,

pakuti ndi Iye yekha amene adzawonjola mapazi anga mu msampha.

16Tembenukirani kwa ine ndipo mundikomere mtima,

pakuti ndili ndekhandekha ndipo ndikuzunzika.

17Masautso a mu mtima mwanga achulukirachulukira;

masuleni ku zowawa zanga.

18Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga

ndipo mufafanize machimo anga onse.

19Onani mmene adani anga achulukira

ndi momwe chidani chawo ndi ine chakulira.

20Tetezani moyo wanga ndi kundilanditsa;

musalole kuti ndichite manyazi,

pakuti ndimathawira kwa Inu.

21Kukhulupirika ndi kulungama kwanga kunditeteze,

chifukwa chiyembekezo changa chili mwa Inu.

22Wombolani Israeli Inu Mulungu,

ku mavuto ake onse!