Nnwom 142 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 142:1-7

Dwom 142

Dawid de. Bere a na ɔwɔ ɔbodan mu no. Mpaebɔ.

1Meteɛ mu su frɛ Awurade;

mema me nne so su frɛ Awurade sɛ onhu me mmɔbɔ.

2Mihwie mʼahiasɛm gu nʼanim;

meka me haw kyerɛ no.

3Sɛ me kra tɔ beraw wɔ me mu a,

ɛyɛ wo na wunim me kwan.

Ɔkwan a menam so no

nnipa asum me afiri.

4Hwɛ na hu, obiara nni me nifa so;

mʼasɛm mfa obiara ho;

minni guankɔbea bi;

me nkwa mfa obiara ho.

5Awurade, misu frɛ wo;

mise, “Wone me guankɔbea,

me kyɛfa wɔ ateasefo asase so.”

6Tie me sufrɛ,

na mewɔ ahohia kɛse mu;

gye me fi mʼataafo nsam,

efisɛ wɔn ho yɛ den sen me.

7Yi me fi mʼafiase,

na makamfo wo din.

Afei atreneefo betwa me ho ahyia

esiane wo papa a woayɛ me no nti.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 142:1-7

Salimo 142

Ndakatulo ya Davide, pamene iyeyo anali mʼphanga. Pemphero.

1Ndikulirira Yehova mofuwula;

ndikukweza mawu anga kwa Yehova kupempha chifundo.

2Ndikukhuthula madandawulo anga pamaso pake;

ndikufotokoza za masautso anga pamaso pake.

3Pamene mzimu wanga walefuka mʼkati mwanga,

ndinu amene mudziwa njira yanga.

Mʼnjira imene ndimayendamo

anthu anditchera msampha mobisa.

4Yangʼanani kumanja kwanga ndipo onani;

palibe amene akukhudzika nane.

Ndilibe pothawira;

palibe amene amasamala za moyo wanga.

5Ndilirira Inu Yehova;

ndikuti, “Ndinu pothawirapo panga,

gawo langa mʼdziko la anthu amoyo.”

6Mverani kulira kwanga

pakuti ndathedwa nzeru;

pulumutseni kwa amene akundithamangitsa

pakuti ndi amphamvu kuposa ine.

7Tulutseni mʼndende yanga

kuti nditamande dzina lanu.

Ndipo anthu olungama adzandizungulira

chifukwa cha zabwino zanu pa ine.