ƆFA A EDI KAN
Nnwom 1–41
Dwom 1
1Nhyira ne onipa a
ontie amumɔyɛfo afotu
na onni nnebɔneyɛfo nhwɛso akyi
na ɔntena fɛwdifo tenabea.
2Na mmom, Awurade mmara sɔ nʼani,
na osusuw ho awia ne anadwo.
3Ɔte sɛ dua a wɔatɛw wɔ asuten ho,
na ɛsow nʼaba ne bere mu a
nʼahaban no nguan da.
Nea ɔyɛ biara yɛ yiye.
4Nanso nnebɔneyɛfo nte saa;
wɔte sɛ ntɛtɛ a
mframa bɔ gu.
5Enti amumɔyɛfo rentumi nnyina atemmu no ano,
na nnebɔneyɛfo nso rentena atreneefo asafo mu.
6Efisɛ Awurade kyerɛ ɔtreneeni kwan
nanso amumɔyɛfo kwan de, ɛbɛyera.
BUKU LOYAMBA
Masalimo 1–41
Salimo 1
1Wodala munthu
amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4Sizitero ndi anthu oyipa!
Iwo ali ngati mungu
umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.