Nnwom 1 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Nnwom 1:1-6

ƆFA A EDI KAN

Nnwom 1–41

Dwom 1

1Nhyira ne onipa a

ontie amumɔyɛfo afotu

na onni nnebɔneyɛfo nhwɛso akyi

na ɔntena fɛwdifo tenabea.

2Na mmom, Awurade mmara sɔ nʼani,

na osusuw ho awia ne anadwo.

3Ɔte sɛ dua a wɔatɛw wɔ asuten ho,

na ɛsow nʼaba ne bere mu a

nʼahaban no nguan da.

Nea ɔyɛ biara yɛ yiye.

4Nanso nnebɔneyɛfo nte saa;

wɔte sɛ ntɛtɛ a

mframa bɔ gu.

5Enti amumɔyɛfo rentumi nnyina atemmu no ano,

na nnebɔneyɛfo nso rentena atreneefo asafo mu.

6Efisɛ Awurade kyerɛ ɔtreneeni kwan

nanso amumɔyɛfo kwan de, ɛbɛyera.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 1:1-6

BUKU LOYAMBA

Masalimo 1–41

Salimo 1

1Wodala munthu

amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,

kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,

kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.

2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova

ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.

3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,

umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake

ndipo masamba ake safota.

Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.

4Sizitero ndi anthu oyipa!

Iwo ali ngati mungu

umene umawuluzidwa ndi mphepo.

5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,

kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.

6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,

koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.