Amos 8 – AKCB & CCL

Akuapem Twi Contemporary Bible

Amos 8:1-14

Kɛntɛn A Aduaba A Abere Wɔ Mu

1Afei nea Otumfo Awurade yi kyerɛɛ me ni: kɛntɛn a aduaba a abere wɔ mu. 2Obisae se, “Dɛn na wuhu, Amos?”

Mibuae se, “Kɛntɛn a wɔde nnuaba a abere ahyɛ no ma.”

Na Awurade ka kyerɛɛ me se, “Me nkurɔfo Israelfo bere no aso; meremfa wɔn ho nkyɛ wɔn bio.”

3Sɛnea Otumfo Awurade se ni, “Saa da no, hyiadan nnwonto bɛdan agyaadwotwa. Wɔbɛbɔ afunu bebree apete baabiara! Enti yɛ komm!”

4Muntie saa asɛm yi, mo a mutiatia mmɔborɔfo so,

na mopam ahiafo fi wɔn asase so,

5na moka se,

“Bere bɛn na ɔsram foforo betwa mu

ama yɛatɔn aduan,

na Homeda bɛba awiei

ama yɛadi awi gua?”

Sɛ mobɛhyɛ susukoraa mu

na moatoto ɔbo so

na mode nsania a wɔamia mu asisi atɔfo,

6na mode dwetɛ atɔ ahiafo

na mmɔborɔfo nso moatɔn wɔn agye mpaboa,

na moapra awi ase afra awi mu atɔn.

7Awurade de Yakob ahohoahoa aka ntam se: “Me werɛ remfi biribiara a wɔayɛ da.

8“Asase renwosow wɔ nea asi yi ho ana,

na wɔn a wɔte mu nyinaa rentwa adwo ana?

Asase no nyinaa bɛma ne ho so te sɛ Nil8.8 Yiri tɛnn te se Nil: Osu a ɛtɔ bere ano bere ano wɔ Etiopia no ma Asubɔnten Nil a ɛwɔ Misraim yiri bu fa so bɛyɛ anammɔn 25 ma ne subon no yɛ ma. Nsuyiri yi soa dɔte pa kogu asase no so.

ebubu afa so, na asan atwe bio

te sɛ Misraim asubɔnten.”

9Sɛnea Otumfo Awurade se ni,

“Saa da no, mɛma owia atɔ owigyinae,

na mama sum aduru asase so awia ketee.

10Mɛdan mo nyamesom aponto ama ayɛ awerɛhowdi

na mo nnwonto nyinaa adan osu.

Mɛma mo nyinaa afura atweaatam

na mayi mo tinwi.

Mɛyɛ saa da no te sɛ ɔba koro ho awerɛhowdida

na awiei no ayɛ sɛ da a ɛyɛ nwen.

11“Nna no reba” sɛnea Otumfo Awurade se ni,

“Mɛma ɔkɔm aba asase no so,

ɛnyɛ aduankɔm anaa osukɔm,

na mmom, Awurade asɛm ho kɔm.

12Nnipa bɛtɔ ntintan akyinkyin afi po so akɔ po so,

na wɔakyinkyin afi atifi fam akɔ apuei fam,

sɛ wɔrekɔhwehwɛ Awurade asɛm,

nanso wɔrenhu.

13“Na saa da no

“mmabaa ahoɔfɛfo ne mmarimaa ahoɔdenfo

bɛtotɔ beraw esiane osukɔm nti.

14Wɔn a wɔde Samaria aniwu abosom ka ntam,

anaa wɔde Dan ne Beer-Seba abosom ka ntam no,

wɔbɛhwehwe ase na wɔrensɔre bio.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amosi 8:1-14

Dengu la Zipatso Zakupsa

1Zimene Ambuye Yehova anandionetsa ndi izi: dengu la zipatso zakupsa. 2Iye anandifunsa kuti, “Amosi nʼchiyani ukuona?”

Ine ndinayankha kuti, “Dengu la zipatso zakupsa.”

Ndipo Yehova anati kwa ine, “Nthawi yachimaliziro yawakwanira anthu anga Aisraeli; sindidzawakhululukiranso.

3“Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akulengeza kuti, “Nyimbo za mʼNyumba ya Mulungu zidzasanduka kulira kofuwula. Mitembo ya anthu idzachuluka, ndipo adzayiponya ponseponse! Kudzangoti zii!”

4Imvani izi, inu amene mumapondereza anthu osowa

ndipo simulabadira anthu osauka a mʼdzikomu.

5Mumanena kuti,

“Kodi chikondwerero cha mwezi watsopano chidzatha liti

kuti tigulitse zinthu?

Ndipo tsiku la Sabata litha liti

kuti tigulitse tirigu,

kuti tichepetse miyeso,

kukweza mitengo

kuti tibere anthu ndi miyeso ya chinyengo,

6tigule osauka ndi ndalama zasiliva

ndi osowa powapatsa nsapato,

tigulitse ngakhale mungu wa tirigu?”

7Yehova amene Yakobo amamunyadira, walumbira kuti: Ine sindidzayiwala chilichonse chimene anachita.

8“Kodi dziko silidzagwedezeka chifukwa cha zimenezi,

ndi onse okhala mʼmenemo kulira mwachisoni?

Dziko lonse lidzavunduka ngati mtsinje wa Nailo;

lidzagwedezeka kenaka nʼkukhala bata

ngati mtsinje wa ku Igupto.

9“Tsiku limenelo,” Ambuye Yehova akunena kuti,

“Ndidzadetsa dzuwa masana

ndi kugwetsa mdima pa dziko lapansi dzuwa likuswa mtengo.

10Maphwando anu achipembedzo ndidzawasandutsa kulira kwa chisoni

ndipo kuyimba kwanu konse ndidzakusandutsa maliro.

Ndidzakuvekani chiguduli nonsenu

ndi kumeta mipala mitu yanu.

Nthawi imeneyo idzakhala ngati yolira mwana wamwamuna mmodzi yekhayo,

ndipo tsikulo lidzakhala lowawa mpaka kutha kwake.

11“Nthawi ikubwera,” Ambuye Yehova akunena kuti,

“Ndidzagwetsa njala mʼdziko lonse;

osati njala ya chakudya kapena ludzu la madzi,

koma njala yofuna kumva mawu a Yehova.

12Anthu azidzangoyendayenda kuchoka ku nyanja ina kupita ku nyanja ina.

Azidzangoyendayenda kuchoka kumpoto kupita kummawa,

kufunafuna mawu a Yehova,

koma sadzawapeza.

13“Tsiku limenelo

“anamwali okongola ndi anyamata amphamvu

adzakomoka ndi ludzu.

14Onse amene amalumbira pa tchimo la Samariya,

kapena kumanena kuti, ‘Iwe Dani, pali mulungu wako wamoyo,’

kapena, ‘Pali mulungu wamoyo wa ku Beeriseba.’

Iwowo adzagwa

ndipo sadzadzukanso.”